-
2 Mbiri 28:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Nawonso Afilisiti+ anaukira mizinda ya Yuda ya ku Sefela+ ndi ku Negebu nʼkulanda mzinda wa Beti-semesi,+ wa Aijaloni+ ndi wa Gederoti. Analandanso mzinda wa Soko ndi midzi yake yozungulira, Timuna+ ndi midzi yake yozungulira komanso wa Gimizo ndi midzi yake yozungulira, ndipo anayamba kukhala kumeneko.
-
-
Yesaya 9:11, 12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Yehova adzakweza adani a Rezini kuti alimbane naye
Ndipo adzachititsa adani a Isiraeli kuti amuukire,
12 Siriya adzachokera kumʼmawa ndipo Afilisiti adzachokera kumadzulo,*+
Iwo adzadya Isiraeli ndi pakamwa potsegula.+
Chifukwa cha zonsezi, mkwiyo wake sunabwerere,
Koma dzanja lake lidakali lotambasula kuti awalange.+
-
-
Yesaya 14:29Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
29 “Usasangalale iwe Filisitiya, kapena aliyense wokhala mwa iwe
Chifukwa chakuti ndodo ya amene ankakumenya yathyoka.
-
-
Yoweli 3:4-6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika