Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Zitatero Yehova Mulungu anadzala munda ku Edeni,+ chakumʼmawa, ndipo mʼmundamo anaikamo munthu amene anamuumba uja.+

  • Ezekieli 28:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Iwe mwana wa munthu, imba nyimbo yoimba polira yokhudza mfumu ya Turo. Uuze mfumuyo kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti:

      “Iwe unali chitsanzo changwiro,

      Unali ndi nzeru zochuluka+ ndiponso wokongola kwambiri.+

      13 Iwe unali mu Edeni, munda wa Mulungu.

      Unakongoletsedwa ndi miyala yamtengo wapatali yamitundu yonse

      Monga rube, topazi, yasipi, kulusolito, onekisi, yade, safiro, nofeki+ ndi emarodi.

      Zoikamo miyala imeneyi zinali zagolide.

      Ndinazipanga pa tsiku limene ndinakulenga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena