Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 18:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Koma iwo sanamvetse tanthauzo la chilichonse cha zimenezi chifukwa mawu amenewa anabisika kwa iwo ndipo sanamvetse zimene zinanenedwazo.

  • Machitidwe 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iye anawayankha kuti: “Simukufunika kudziwa nthawi kapena nyengo imene Atate wasankha mu ulamuliro wake.+

  • 1 Petulo 1:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Aneneri amene analosera za kukoma mtima kwakukulu kumene Mulungu anakusonyezani, anafufuza za chipulumutso chimenechi mwakhama ndiponso mosamala kwambiri.+ 11 Mzimu woyera unali utaneneratu kuti Khristu+ adzavutika ndipo kenako adzalandira ulemerero. Aneneri ankafufuza zizindikiro zimene mzimu woyera* unawasonyeza zokhudza nthawi yeniyeni komanso nyengo imene zimenezi zidzachitike.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena