Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 24:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Chisautso cha masiku amenewo chikadzangotha, dzuwa lidzachita mdima+ ndipo mwezi sudzapereka kuwala kwake. Nyenyezi zidzagwa kuchokera kumwamba ndipo mphamvu zakumwamba zidzagwedezeka.+

  • Maliko 13:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Koma mʼmasiku amenewo, chisautso chimenecho chikadzangotha, dzuwa lidzachita mdima ndipo mwezi sudzapereka kuwala kwake.+ 25 Nyenyezi zidzagwa kuchokera kumwamba ndipo mphamvu zimene zili kumwamba zidzagwedezeka.

  • Luka 21:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Komanso padzakhala zizindikiro padzuwa, mwezi ndi nyenyezi.+ Padziko lapansi anthu a mitundu ina adzazunzika chifukwa chothedwa nzeru poona kuti nyanja ikuchita mkokomo komanso kuwinduka.

  • Chivumbulutso 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Atamatula chidindo cha 6, ndinaona kuti kunachitika chivomerezi chachikulu. Dzuwa linada ngati chiguduli choluka ndi ubweya* ndipo mwezi wonse unafiira ngati magazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena