Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mʼmasiku otsiriza,

      Phiri la nyumba ya Yehova

      Lidzakhazikika pamwamba penipeni pa mapiri akuluakulu,+

      Ndipo lidzakwezedwa kupitirira mapiri angʼonoangʼono.

      Anthu a mitundu yonse adzapita kumeneko.+

  • Yesaya 11:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Sizidzavulazana+

      Kapena kuwonongana mʼphiri langa lonse loyera,+

      Chifukwa dziko lapansi lidzadzaza ndi anthu odziwa Yehova

      Ngati mmene madzi amadzazira mʼnyanja.+

  • Yesaya 66:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Adzabweretsa abale anu onse kuchokera ku mitundu yonse+ ngati mphatso kwa Yehova. Adzawabweretsa atakwera mahatchi, ngolo, ngolo zotseka pamwamba, nyulu* ndi ngamila zothamanga, mpaka kukafika kuphiri langa loyera, ku Yerusalemu. Adzachita zimenezi ngati mmene Aisiraeli amabweretsera mphatso mʼnyumba ya Yehova, ataiika mʼchiwiya choyera,” akutero Yehova.

  • Yeremiya 31:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: “Ndikadzasonkhanitsa anthu a mtundu wawo amene anagwidwa nʼkutengedwa kupita kudziko lina, iwo adzanenanso mawu awa mʼdziko la Yuda ndi mʼmizinda yake kuti, ‘Yehova akudalitse iwe malo olungama okhalamo,+ iwe phiri lopatulika.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena