-
Yesaya 2:2, 3Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Mʼmasiku otsiriza,
Phiri la nyumba ya Yehova
Lidzakhazikika pamwamba penipeni pa mapiri akuluakulu,+
Ndipo lidzakwezedwa kupitirira mapiri angʼonoangʼono.
Anthu a mitundu yonse adzapita kumeneko.+
3 Anthu ochokera mʼmitundu yosiyanasiyana adzabwera nʼkunena kuti:
“Bwerani. Tiyeni tipite kukakwera phiri la Yehova,
Tipite kunyumba ya Mulungu wa Yakobo.+
Iye akatiphunzitsa njira zake,
Ndipo ife tidzayenda mʼnjira zakezo.”+
-
-
Mika 4:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Anthu ochokera mʼmitundu yosiyanasiyana adzabwera nʼkunena kuti:
“Bwerani, tiyeni tipite kuphiri la Yehova,
Tipite kunyumba ya Mulungu wa Yakobo.+
Iye akatiphunzitsa njira zake,
Ndipo ife tidzayenda mʼnjira zakezo.”
Chifukwa chilamulo,* chidzaphunzitsidwa mu Ziyoni
Ndipo mawu a Yehova adzaphunzitsidwa mu Yerusalemu.
-