Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 31:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Iwo adzabwera akulira.+

      Ndidzawatsogolera akadzandipempha kuti ndiwakomere mtima.

      Ndidzawatsogolera kumitsinje ya madzi,*+

      Ndipo ndidzawayendetsa mʼnjira yabwino imene sadzapunthwa.

      Chifukwa ine ndine Bambo ake a Isiraeli ndipo Efuraimu ndi mwana wanga woyamba kubadwa.”+

  • Yeremiya 31:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Kodi Efuraimu si mwana wanga wamtengo wapatali, amene ndimamukonda?+

      Ngakhale kuti nthawi zambiri ndimamudzudzula, ndimamukonda ndipo ndimamukumbukirabe.

      Nʼchifukwa chake ndakhudzika naye* kwambiri.+

      Ndipo sindidzalephera kumumvera chisoni,” akutero Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena