Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 10:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mayina a atumwi 12 ndi awa:+ Simoni, amene ankatchulidwa kuti Petulo*+ ndi Andireya+ mchimwene wake. Yakobo mwana wa Zebedayo ndi mchimwene wake Yohane.+

  • Mateyu 27:55, 56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Komanso azimayi ambiri ochokera ku Galileya amene ankatsatira Yesu kuti azimutumikira, anali komweko nʼkumaonerera chapatali.+ 56 Ena mwa iwo anali Mariya wa ku Magadala, Mariya mayi a Yakobo ndi Yose, ndiponso panali mayi a Yakobo ndi Yohane.*+

  • Maliko 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Yakobo mwana wa Zebedayo ndi Yohane mchimwene wake wa Yakobo (awiriwa anawapatsanso dzina lakuti Boanege, limene limatanthauza “Ana a Bingu”),+

  • Maliko 10:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ndiyeno Yakobo ndi Yohane, ana aamuna a Zebedayo,+ anapita kwa iye nʼkumuuza kuti: “Mphunzitsi, tikufuna kuti mutichitire chilichonse chimene tingakupempheni.”+

  • Yohane 21:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Simoni Petulo, Tomasi (amene ankatchulidwa kuti Didimo),+ Natanayeli+ wa ku Kana wa ku Galileya, ana a Zebedayo+ ndi ophunzira ake ena awiri onsewa anali pamodzi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena