Mateyu 19:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ine ndikukuuzani kuti aliyense amene wasiya mkazi wake nʼkukwatira wina wachita chigololo, kupatulapo ngati wamusiya chifukwa cha chiwerewere.”*+ Maliko 10:11, 12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Iye anawauza kuti: “Aliyense amene wasiya mkazi wake nʼkukwatira wina, wachita chigololo+ ndipo walakwira mkaziyo. 12 Ndipo ngati mkazi wasiya mwamuna wake nʼkukwatiwa ndi wina, wachita chigololo.”+ Luka 16:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Aliyense amene wasiya mkazi wake nʼkukwatira wina, wachita chigololo ndipo aliyense amene wakwatira mkazi wosiyidwayo nayenso wachita chigololo.+ Aroma 7:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ngati mkaziyo angakwatiwe ndi mwamuna wina mwamuna wake ali moyo, ndiye kuti wachita chigololo.+ Koma ngati mwamuna wake wamwalira, mkaziyo wamasuka ku lamulo lokhudza mwamuna wake, choncho sanachite chigololo ngati atakwatiwa ndi mwamuna wina.+
9 Ine ndikukuuzani kuti aliyense amene wasiya mkazi wake nʼkukwatira wina wachita chigololo, kupatulapo ngati wamusiya chifukwa cha chiwerewere.”*+
11 Iye anawauza kuti: “Aliyense amene wasiya mkazi wake nʼkukwatira wina, wachita chigololo+ ndipo walakwira mkaziyo. 12 Ndipo ngati mkazi wasiya mwamuna wake nʼkukwatiwa ndi wina, wachita chigololo.”+
18 Aliyense amene wasiya mkazi wake nʼkukwatira wina, wachita chigololo ndipo aliyense amene wakwatira mkazi wosiyidwayo nayenso wachita chigololo.+
3 Ngati mkaziyo angakwatiwe ndi mwamuna wina mwamuna wake ali moyo, ndiye kuti wachita chigololo.+ Koma ngati mwamuna wake wamwalira, mkaziyo wamasuka ku lamulo lokhudza mwamuna wake, choncho sanachite chigololo ngati atakwatiwa ndi mwamuna wina.+