Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 4:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Maso ako aziyangʼana patsogolo.

      Inde, uziyangʼanitsitsa* zinthu zimene zili patsogolo pako.+

  • Luka 11:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Nyale ya thupi ndi diso lako. Ngati diso lako likuyangʼana* pachinthu chimodzi, thupi lako lonse lidzakhalanso lowala kwambiri. Koma ngati lili ladyera,* thupi lako lonse lidzachitanso mdima.+

  • Aefeso 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mulungu watsegula mitima yanu nʼcholinga choti muone komanso mudziwe chiyembekezo chimene wakupatsani ndiponso zinthu zabwino kwambiri zimene walonjeza kwa oyera,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena