Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 6:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Nyale ya thupi ndi diso.+ Choncho ngati diso lako likuyangʼana* pachinthu chimodzi, thupi lako lonse lidzakhala lowala kwambiri. 23 Koma ngati diso lako lili ladyera,*+ thupi lako lonse lidzachita mdima. Choncho ngati kuwala kumene kuli mwa iwe ndi mdima, ndiye kuti mdimawo ndi wandiweyani!

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena