Mateyu 12:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Ali mkati molankhula ndi gulu la anthulo, kunabwera mayi ake ndi azichimwene ake.+ Iwo anaima panja ndipo ankafuna kuti alankhule naye.+ Yohane 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Zimenezi zitachitika, Yesu, mayi ake, azichimwene ake+ ndi ophunzira ake anapita ku Kaperenao,+ koma sanakhaleko masiku ambiri. Machitidwe 1:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Mogwirizana, onsewa ankalimbikira kupemphera pamodzi ndi Mariya mayi a Yesu, azimayi ena+ komanso azichimwene ake a Yesu.+ 1 Akorinto 9:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Kodi tilibe ufulu woyenda limodzi ndi akazi athu okhulupirira+ ngati mmene amachitira atumwi ena onse, abale awo a Ambuye+ komanso Kefa?*+ Agalatiya 1:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Koma atumwi ena onse sindinawaone kupatulapo Yakobo,+ mchimwene wa Ambuye.
46 Ali mkati molankhula ndi gulu la anthulo, kunabwera mayi ake ndi azichimwene ake.+ Iwo anaima panja ndipo ankafuna kuti alankhule naye.+
12 Zimenezi zitachitika, Yesu, mayi ake, azichimwene ake+ ndi ophunzira ake anapita ku Kaperenao,+ koma sanakhaleko masiku ambiri.
14 Mogwirizana, onsewa ankalimbikira kupemphera pamodzi ndi Mariya mayi a Yesu, azimayi ena+ komanso azichimwene ake a Yesu.+
5 Kodi tilibe ufulu woyenda limodzi ndi akazi athu okhulupirira+ ngati mmene amachitira atumwi ena onse, abale awo a Ambuye+ komanso Kefa?*+