Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 1:23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pa nthawiyo, mʼsunagoge mwawomo munali munthu wogwidwa ndi mzimu wonyansa, ndipo munthuyo anafuula kuti: 24 “Kodi mukufuna chiyani kwa ife, inu Yesu Mnazareti?+ Kodi mwabwera kudzatiwononga? Inetu ndikukudziwani bwino kwambiri, ndinu Woyera wa Mulungu!”+

  • Maliko 5:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako anafuula ndi mawu amphamvu kuti: “Kodi mukufuna chiyani kwa ine, Yesu, Mwana wa Mulungu Wamʼmwambamwamba? Ndikukulumbiritsani pali Mulungu kuti musandizunze.”+

  • Luka 4:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ziwanda nazonso zinatuluka mwa anthu ambiri zikufuula kuti: “Inu ndinu Mwana wa Mulungu.”+ Koma iye anadzudzula ziwandazo ndipo sanazilole kuti zilankhule+ chifukwa zinkamudziwa kuti ndi Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena