Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndidzatsegula pakamwa panga nʼkunena mwambi.

      Ndidzanena mawu ophiphiritsa akalekale.+

  • Mateyu 13:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu analankhula zonsezi ndi gulu la anthulo pogwiritsa ntchito mafanizo. Ndithudi, nthawi zonse iye ankalankhula nawo pogwiritsa ntchito mafanizo,+ 35 kuti zimene Mulungu ananena kudzera mwa mneneri zikwaniritsidwe. Mneneriyo anati: “Ndidzatsegula pakamwa panga nʼkunena mafanizo. Ndidzafalitsa zinthu zimene zinabisika kuchokera pachiyambi.”*+

  • Maliko 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndithudi, nthawi zonse iye ankalankhula nawo pogwiritsa ntchito mafanizo, koma kumbali ankafotokoza zinthu zonse kwa ophunzira ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena