Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 49:16-19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Musachite mantha chifukwa chakuti munthu wina walemera,

      Kapena chifukwa chakuti katundu wamʼnyumba mwake wawonjezeka,

      17 Chifukwa akadzamwalira sadzatenga china chilichonse.+

      Ulemerero wake sadzapita nawo limodzi.+

      18 Chifukwa pamene anali moyo ankatamanda moyo wake.+

      (Anthu amakutamanda ukalemera.)+

      19 Koma pamapeto pake amafa ngati mmene makolo ake anachitira.

      Iwo sadzaonanso kuwala.

  • Miyambo 27:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Usadzitame ndi zimene udzachite mawa

      Chifukwa sukudziwa zimene zidzachitike mawa.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena