Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 24:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Choncho khalanibe maso chifukwa simukudziwa tsiku limene Ambuye wanu adzabwere.+

  • Maliko 13:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Choncho khalanibe maso chifukwa simukudziwa nthawi imene mwininyumba adzabwere.+ Simukudziwa ngati adzabwere madzulo, pakati pa usiku, mʼmbandakucha* kapena mʼmamawa,+

  • Chivumbulutso 6:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Iwo ankauza mapiri ndi matanthwe kuti: “Tigwereni,+ tibiseni kuti tisaonekere kwa Mulungu amene wakhala pampando wachifumu+ ndiponso kuti mkwiyo wa Mwanawankhosa usatigwere,+ 17 chifukwa tsiku lalikulu la mkwiyo wawo lafika,+ ndipo ndi ndani amene angaimirire pamaso pawo?”+

  • Chivumbulutso 16:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Taona! Ndikubwera ngati wakuba.+ Wosangalala ndi amene akukhalabe maso+ ndiponso amene wavalabe malaya ake akunja, kuti asayende wosavala anthu nʼkuona maliseche ake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena