-
Machitidwe 8:35Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
35 Zitatero, Filipo anayamba kumuuza uthenga wabwino wonena za Yesu, ndipo anayambira palemba lomweli.
-
-
1 Petulo 1:18, 19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Mukudziwa inu kuti zinthu zimene zinakumasulani*+ ku moyo wanu wopanda phindu umene munatengera kuchokera kwa makolo anu, sizinali zinthu zotha kuwonongeka monga siliva kapena golide. 19 Koma munamasulidwa ndi magazi amtengo wapatali+ a Khristu,+ omwe ndi ofanana ndi magazi a nkhosa yopanda chilema komanso yopanda mawanga.+
-