Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Akudya chakudyacho iye ananena kuti: “Ndithu ndikukuuzani, mmodzi wa inu andipereka.”+

  • Maliko 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndipo atakhala patebulo nʼkumadya chakudya, Yesu anati: “Ndithu ndikukuuzani, mmodzi wa inu, amene akudya nane limodzi, andipereka.”+

  • Luka 22:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma taonani! Wondipereka ndili naye limodzi patebulo pompano.+

  • Yohane 6:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 Yesu anawauza kuti: “Ine ndinakusankhani inu 12, si choncho?+ Komatu mmodzi wa inu ndi wonenera anzake zoipa.”*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena