Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Moyo unakhalapo kudzera mwa iye ndipo moyowo unali kuwala kounikira anthu.+

  • Yohane 6:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Mzimu ndi umene umapatsa moyo+ koma mnofu ulibe ntchito iliyonse. Mawu amene ndakuuzaniwa ndi mzimu ndiponso ndi moyo.+

  • Yohane 17:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Moyo wosatha adzaupeza+ akamaphunzira ndi kudziwa za inu, Mulungu yekhayo amene ndi woona,+ komanso za Yesu Khristu, amene inu munamutuma.+

  • Aroma 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chifukwa malipiro a uchimo ndi imfa,+ koma mphatso imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha+ kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye wathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena