Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 2:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Komanso Simiyoni anadalitsa makolowo ndipo anauza Mariya, mayi a mwanayo kuti: “Tamvera! Mwanayu waikidwa kuti ambiri agwe+ ndiponso kuti ambiri adzukenso mu Isiraeli.+ Komanso kuti akhale chizindikiro chimene anthu adzachitsutse+ 35 (inde, lupanga lalitali lidzakubaya)+ kuti zimene anthu ambiri akuganiza mumtima mwawo zionekere poyera.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena