Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 12:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Pamene kuwala mudakali nako, sonyezani kuti mukukhulupirira kuwalako, kuti mukhale ana ake a kuwala.”+

      Yesu atanena zimenezi, anachoka nʼkukabisala.

  • Yohane 12:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Ndabwera monga kuwala mʼdziko,+ kuti aliyense wokhulupirira ine asapitirize kukhala mumdima.+

  • 1 Yohane 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Komatu ngati tikuyenda mʼkuwala mofanana ndi mmenenso iye alili mʼkuwala, ndiye kuti ndife ogwirizana ndipo magazi a Yesu, yemwe ndi Mwana wake, akutiyeretsa ku machimo onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena