Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 Apanso Petulo anakana. Patapita kanthawi pangʼono, amene anali ataimirira chapafupi anayambanso kuuza Petulo kuti: “Ndithu iwenso uli mʼgulu la ophunzira ake. Ndipo ndiwenso Mgalileya.”

  • Machitidwe 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Azibambowo anawafunsa kuti: “Amuna inu a ku Galileya, nʼchifukwa chiyani mwangoima nʼkumayangʼana kumwamba? Yesu, amene watengedwa pakati panu kupita kumwambayu, adzabwera mʼnjira yofanana ndi mmene mwamuonera akupita kumwamba.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena