Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 5:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Musaganize kuti ndinabwera kudzawononga Chilamulo kapena zimene aneneri analemba. Sindinabwere kudzaziwononga koma kudzazikwaniritsa.+

  • Aroma 8:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chilamulo chinalibe mphamvu yokumasulani+ chifukwa anthu ndi ofooka+ komanso ochimwa. Koma kuti akumasuleni, Mulungu anatumiza Mwana wake+ ali ndi thupi ngati la anthu ochimwa+ kuti athane ndi uchimo. Choncho Mulungu anagonjetsa uchimo pogwiritsa ntchito thupi. 4 Mulungu anachita izi kuti ife amene timayenda motsatira mzimu, osati motsatira zofuna za thupi,+ tikwaniritse zinthu zolungama zimene Chilamulo chimafuna.+

  • Aroma 13:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chikondi sichilimbikitsa munthu kuchitira mnzake zoipa,+ choncho chikondi chimathandiza munthu kuti akwaniritse lamulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena