Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Akorinto 5:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma zinthu zonse nʼzochokera kwa Mulungu, amene anatithandiza kuti tigwirizane naye kudzera mwa Khristu,+ ndipo anatipatsa utumiki wothandiza kuti anthu agwirizanenso ndi Mulungu.+

  • Akolose 1:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndithudi, inu amene kale munali otalikirana ndi Mulungu ndiponso adani ake chifukwa maganizo anu anali pa ntchito zoipa, 22 tsopano wagwirizana nanunso kudzera mu imfa ya mwana wake amene anapereka thupi lake lanyama nʼcholinga choti akuperekeni pamaso pa Mulunguyo, muli opatulika ndi opanda chilema ndiponso opanda chifukwa chokunenezerani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena