Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ngati tinagwirizanitsidwa ndi Mulungu kudzera mu imfa ya Mwana wake+ pa nthawi imene tinali adani, ndiye kuti tidzapulumutsidwa ndithu ndi moyo wake, popeza panopa tagwirizanitsidwa.

  • Aefeso 2:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndi thupi lake, anathetsa chinthu choyambitsa chidani, chomwe ndi Chilamulo chimene chinali ndi malamulo komanso malangizo. Anachithetsa kuti magulu awiri omwe ndi ogwirizana ndi iye, akhale munthu mmodzi watsopano+ komanso kuti akhazikitse mtendere. 16 Ndiponso kuti kudzera mwa mtengo wozunzikirapo,*+ agwirizanitse magulu awiri a anthuwo kwa Mulungu ndipo anthuwo akhale thupi limodzi, chifukwa anali atapheratu chidanicho+ kudzera mu imfa yake.

  • Akolose 1:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Zili choncho chifukwa chakuti Mulungu zinamusangalatsa kuti makhalidwe ake onse akhale mwa Khristu.+ 20 Komanso kuti kudzera mwa mwana wakeyo agwirizanitsenso zinthu zina zonse+ ndi iyeyo, kaya zinthuzo ndi zapadziko lapansi kapena zakumwamba. Anachita zimenezi pokhazikitsa mtendere kudzera mʼmagazi+ amene Khristu anakhetsa pamtengo wozunzikirapo.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena