Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 30:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Chifukwa mawu a chilamulowo ali pafupi kwambiri ndi inu, ali mʼkamwa mwanu ndi mumtima mwanu+ kuti muwatsatire.+

  • Ezekieli 20:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako ndinawapatsa malamulo anga ndi kuwadziwitsa zigamulo zanga+ kuti munthu amene akuzitsatira akhale ndi moyo.+

  • Yakobo 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Komabe muzichita zimene mawu amanena,+ osati kungomva chabe, nʼkumadzipusitsa ndi maganizo abodza.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena