Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Atate saweruza munthu aliyense, koma wapereka udindo wonse woweruza kwa Mwana,+

  • Machitidwe 10:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Ndiponso, anatilamula kuti tilalikire kwa anthu ndi kupereka umboni wokwanira+ woti iyeyu ndi amene Mulungu anamupatsa udindo woweruza anthu amoyo ndi akufa.+

  • 1 Petulo 4:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma anthu amenewa adzayankha mlandu kwa Khristu yemwe adzaweruze amoyo ndi akufa omwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena