Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 3:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mʼmibadwo yamʼmbuyo, chinsinsi chimenechi sichinaululidwe kwa ana a anthu mmene Mulungu wachiululira panopa kwa atumwi ndi aneneri ake oyera kudzera mwa mzimu.+ 6 Chinsinsi chimenechi nʼchakuti anthu a mitundu ina amene ndi ogwirizana ndi Khristu Yesu, adzalandire cholowa chimene Khristu adzalandire, ndipo adzakhala mbali ya thupi.+ Iwo adzalandiranso zinthu zimene Mulungu watilonjeza chifukwa cha uthenga wabwino.

  • Akolose 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndikuchita zimenezi kuti mitima yawo ilimbikitsidwe+ ndiponso kuti onse akhale ogwirizana mʼchikondi+ komanso kuti alandire chuma chonse chimene chimabwera chifukwa chomvetsa bwino zinthu, popanda kukayikira chilichonse, nʼcholinga choti adziwe molondola chinsinsi chopatulika cha Mulungu, chomwe ndi Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena