Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Agalatiya 1:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chifukwa ndikufuna kuti mudziwe abale, kuti uthenga wabwino umene ndinalengeza kwa inu sunachokere kwa anthu.+ 12 Uthengawu sindinaulandire kwa munthu ndipo sindinachite kuphunzitsidwa, koma Yesu Khristu ndi amene anandiululira uthenga umenewu.

  • Agalatiya 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndinapita kumeneko chifukwa ndinauzidwa mʼmasomphenya kuti ndipiteko. Ndipo abale ndinawafotokozera uthenga wabwino umene ndikuulalikira kwa anthu a mitundu ina. Koma ndinachita zimenezi mwachinsinsi kwa abale odalirika okha pofuna kutsimikizira kuti utumiki wanga sukupita pachabe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena