-
Yesaya 45:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Yehova wanena kuti:
“Phindu la ku Iguputo,* malonda* a ku Itiyopiya ndi Asabeya, anthu ataliatali,
Adzabwera kwa iwe ndipo adzakhala ako.
Iwo adzayenda pambuyo pako atamangidwa mʼmaunyolo
Adzabwera nʼkudzakugwadira.+
Adzapemphera kwa iwe kuti, ‘Zoonadi Mulungu ali ndi iwe,+
Ndipo palibenso wina. Palibenso Mulungu wina.’”
-