Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Koma Mulungu anamuukitsa+ pomumasula ku zopweteka* za imfa, chifukwa zinali zosatheka kuti imfa imugwire mwamphamvu.+

  • Machitidwe 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 dziwani nonsenu ndi Aisiraeli onse, kuti mʼdzina la Yesu Khristu wa ku Nazareti uja,+ amene inu munamuphera pamtengo,+ koma amene Mulungu anamuukitsa,+ kudzera mwa iyeyo munthuyu waima patsogolo panu ali bwinobwino.

  • Machitidwe 13:30, 31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Koma Mulungu anamuukitsa.+ 31 Ndipo kwa masiku ambiri anaonekera kwa anthu amene anayenda naye kuchokera ku Galileya kupita ku Yerusalemu. Panopa amenewa ndi mboni zake kwa anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena