Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma inuyo, chitani zinthu mwamphamvu ndipo musagwe ulesi,+ popeza mudzapeza mphoto chifukwa cha ntchito yanu.”

  • 1 Akorinto 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Wodzala ndi wothirira amagwira ntchito ali ndi cholinga chimodzi, koma aliyense adzalandira mphoto mogwirizana ndi ntchito yake.+

  • Chivumbulutso 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako ndinamva mawu kuchokera kumwamba akuti, “Lemba kuti: Osangalala ndi anthu amene akufa ali ogwirizana ndi Ambuye+ kuyambira pa nthawi ino kupita mʼtsogolo. Mzimu ukuti asiyeni apume ku ntchito yawo imene anaigwira mwakhama, chifukwa zimene anachita zikupita nawo limodzi.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena