Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 10:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Munthu wochita zinthu mokhulupirika adzakhala wotetezeka,+

      Koma munthu wochita zinthu mwachinyengo adzadziwika.+

  • 2 Akorinto 10:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chifukwa amene amavomerezedwa si wodzikweza,+ koma amene Yehova* wamuvomereza.+

  • 1 Timoteyo 5:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Machimo a anthu ena amadziwika kwa anthu, ndipo amaweruzidwa nthawi yomweyo. Koma anthu ena, machimo awo amadzaonekera pakapita nthawi.+ 25 Nazonso ntchito zabwino zimadziwika kwa anthu,+ ndipo zimene sizidziwika sizingabisike mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena