Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 28:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Aliyense amene amapereka zinthu zake kwa anthu osauka sadzasowa kanthu,+

      Koma amene amatseka maso ake kuti asaone osaukawo adzalandira matemberero ambiri.

  • Malaki 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Bweretsani gawo limodzi pa magawo 10 alionse* a zinthu zanu nʼkuziika mosungiramo zinthu zanga,+ kuti mʼnyumba mwanga mukhale chakudya.+ Ndiyeseni chonde pa nkhani imeneyi, kuti muone ngati sindidzakutsegulirani mageti akumwamba+ nʼkukukhuthulirani madalitso mpaka simudzasowa kanthu,”+ watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba.

  • Afilipi 4:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Komabe, ine ndili ndi zonse zimene ndikufunikira ndipo zikuposa pa zimene ndikufunikira. Sindikusowa kanthu chifukwa Epafurodito+ wandipatsa zinthu zimene mwanditumizira. Zinthu zimenezi zili ngati fungo lonunkhira bwino+ ndiponso nsembe yovomerezeka yomwe ndi yosangalatsa kwa Mulungu. 19 Chifukwa cha zimenezi, Mulungu wanga adzakupatsani zonse zimene mukufunikira+ mogwirizana ndi kuchuluka kwa chuma chake chaulemerero, kudzera mwa Khristu Yesu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena