-
Akolose 1:19, 20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Zili choncho chifukwa chakuti Mulungu zinamusangalatsa kuti makhalidwe ake onse akhale mwa Khristu.+ 20 Komanso kuti kudzera mwa mwana wakeyo agwirizanitsenso zinthu zina zonse+ ndi iyeyo, kaya zinthuzo ndi zapadziko lapansi kapena zakumwamba. Anachita zimenezi pokhazikitsa mtendere kudzera mʼmagazi+ amene Khristu anakhetsa pamtengo wozunzikirapo.*
-