Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Atesalonika 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Komabe, tiyenera kumathokoza Mulungu nthawi zonse chifukwa cha inu, abale amene Yehova* amakukondani, chifukwa Mulungu anakusankhani kuchokera pachiyambi+ kuti mudzapulumuke. Anachita zimenezi pokuyeretsani+ ndi mzimu wake komanso chifukwa munakhulupirira choonadi.

  • 1 Petulo 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndikulembera inu amene Mulungu Atate+ anadziwiratu za inu. Iye anakupatsani mzimu wake kuti mukhale oyera.+ Anachita zimenezi kuti mukhale omvera komanso kuti akuyeretseni ndi magazi a Yesu Khristu.+

      Ndikupempha Mulungu kuti akusonyezeni chifundo chake chachikulu komanso kuti mukhale ndi mtendere.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena