Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 6:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Akapolo inu, muzimvera anthu amene ndi ambuye anu.+ Muziwaopa ndi kuwalemekeza kuchokera pansi pa mtima, ngati mmene mumachitira ndi Khristu. 6 Musamachite zimenezi pokhapokha pamene anthu akukuonani pongofuna kuwasangalatsa,*+ koma ngati akapolo a Khristu amene akuchita chifuniro cha Mulungu ndi mtima wonse.+

  • Tito 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Akapolo azigonjera ambuye awo pa zinthu zonse+ ndipo aziwakondweretsa. Asamatsutsane nawo

  • 1 Petulo 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Antchito azigonjera mabwana awo ndipo aziwalemekeza kwambiri.+ Asamachite zimenezi kwa mabwana abwino ndi ololera okha, koma ngakhalenso kwa ovuta kuwakondweretsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena