Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 19:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Zitatero mumzindawo munadzaza chisokonezo, ndipo anthu onse anathamangira mʼbwalo lamasewera, atagwira Gayo ndi Arisitako+ nʼkuwakokera mʼbwalomo. Gayo ndi Arisitako ankayenda ndi Paulo ndipo kwawo kunali ku Makedoniya.

  • Machitidwe 20:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa ulendowu anali limodzi ndi Sopaturo mwana wa Puro wa ku Bereya, Arisitako+ ndi Sekundo a ku Tesalonika, Gayo wa ku Debe ndi Timoteyo,+ koma ochokera mʼchigawo cha Asia anali Tukiko+ ndi Terofimo.+

  • Machitidwe 27:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ku Adiramutiyo tinakwera ngalawa imene inali itatsala pangʼono kunyamuka ulendo wopita kumadoko amʼmbali mwa nyanja mʼchigawo cha Asia. Kenako tinanyamuka limodzi ndi Arisitako,+ yemwe anali wa ku Makedoniya ku Tesalonika.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena