Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 12:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Atazindikira zimenezi, iye anapita kunyumba kwa Mariya, mayi ake a Yohane wotchedwanso Maliko.+ Kumeneko anthu ambiri anali atasonkhana nʼkumapemphera.

  • Machitidwe 15:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Baranaba ankafunitsitsa kuti atenge Yohane, wotchedwanso Maliko.+

  • Filimoni 23, 24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Epafura,+ mkaidi mnzanga mwa Khristu Yesu, akupereka moni. 24 Maliko, Arisitako,+ Dema+ ndi Luka,+ omwe ndi antchito anzanga, akuperekanso moni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena