Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 2:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kukhala Myuda weniweni kuli mumtima+ ndipo mdulidwe wake umakhalanso wamumtima+ wochitidwa ndi mzimu, osati ndi malamulo olembedwa.+ Munthu woteroyo amatamandidwa ndi Mulungu, osati anthu.+

  • Afilipi 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chifukwa ife tinachita mdulidwe weniweni,+ ife amene tikuchita utumiki wopatulika motsogoleredwa ndi mzimu wa Mulungu. Timadzitamandira mwa Khristu Yesu+ ndipo sitidalira zinthu zimene anthu amaziona kuti ndi zofunika,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena