Machitidwe 20:29, 30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Ndikudziwa kuti ine ndikachoka, mimbulu yopondereza idzafika pakati panu+ ndipo sidzasamalira gulu la nkhosa mwachikondi. 30 Ndipo pakati panu anthu ena adzayamba kulankhula zinthu zopotoka kuti apatutse ophunzira aziwatsatira.+ 1 Akorinto 11:18, 19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Choyamba, ndamva kuti mukasonkhana mumpingo, pakumakhala kugawanika, ndipo kumbali ina ndikuona kuti ndi zoona. 19 Payeneradi kukhala magulu ampatuko pakati panu,+ kuti anthu ovomerezeka kwa Mulungu adziwike. 1 Yohane 2:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Ana inu, ino ndi nthawi yakumapeto. Munamva kuti wokana Khristu akubwera,+ ndipo panopa okana Khristu ambiri aonekera.+ Chifukwa cha zimenezi tikudziwa kuti ino ndi nthawi yakumapeto.
29 Ndikudziwa kuti ine ndikachoka, mimbulu yopondereza idzafika pakati panu+ ndipo sidzasamalira gulu la nkhosa mwachikondi. 30 Ndipo pakati panu anthu ena adzayamba kulankhula zinthu zopotoka kuti apatutse ophunzira aziwatsatira.+
18 Choyamba, ndamva kuti mukasonkhana mumpingo, pakumakhala kugawanika, ndipo kumbali ina ndikuona kuti ndi zoona. 19 Payeneradi kukhala magulu ampatuko pakati panu,+ kuti anthu ovomerezeka kwa Mulungu adziwike.
18 Ana inu, ino ndi nthawi yakumapeto. Munamva kuti wokana Khristu akubwera,+ ndipo panopa okana Khristu ambiri aonekera.+ Chifukwa cha zimenezi tikudziwa kuti ino ndi nthawi yakumapeto.