Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Timoteyo 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Gwiritsitsabe chitsanzo cha mawu olondola+ amene unawamva kwa ine pamene ukusonyeza chikhulupiriro ndi chikondi zomwe timakhala nazo chifukwa chogwirizana ndi Khristu Yesu.

  • Tito 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Popeza ndi mtumiki* wa Mulungu, woyangʼanira ayenera kukhala wopanda chifukwa chomunenezera. Asakhale womva zake zokha,+ wa mtima wapachala,+ womwa mowa mwauchidakwa, wankhanza* kapena wokonda kupeza phindu mwachinyengo.

  • Tito 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Akhalenso wogwira mwamphamvu mawu okhulupirika pamene akuphunzitsa mwaluso,+ kuti athe kulimbikitsa anthu ndi mfundo zolondola+ ndiponso kudzudzula+ otsutsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena