1 Timoteyo 4:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Nthawi zonse uzisamala ndi zimene umachita komanso zimene umaphunzitsa.+ Pitiriza kuchita zimenezi, chifukwa ukatero udzadzipulumutsa wekha komanso anthu okumvera.+ 2 Timoteyo 1:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Gwiritsitsabe chitsanzo cha mawu olondola+ amene unawamva kwa ine pamene ukusonyeza chikhulupiriro ndi chikondi zomwe timakhala nazo chifukwa chogwirizana ndi Khristu Yesu.
16 Nthawi zonse uzisamala ndi zimene umachita komanso zimene umaphunzitsa.+ Pitiriza kuchita zimenezi, chifukwa ukatero udzadzipulumutsa wekha komanso anthu okumvera.+
13 Gwiritsitsabe chitsanzo cha mawu olondola+ amene unawamva kwa ine pamene ukusonyeza chikhulupiriro ndi chikondi zomwe timakhala nazo chifukwa chogwirizana ndi Khristu Yesu.