Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma mmene zilili ndi mphatsoyi, si mmene zinalili ndi uchimowo. Anthu ambiri anafa chifukwa cha uchimo wa munthu mmodzi. Koma kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu ndiponso mphatso yake yaulere imene anaipereka mokoma mtima kudzera mwa munthu mmodzi,+ Yesu Khristu, nʼzapamwamba kwambiri. Pogwiritsa ntchito mphatso imeneyi, Mulungu adzapereka madalitso osaneneka kwa anthu ambiri.+

  • Aroma 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa chiyani? Kuti mmene uchimo unalamulira ngati mfumu pamodzi ndi imfa,+ nakonso kukoma mtima kwakukulu kulamulire ngati mfumu kudzera mʼchilungamo. Ndipo zimenezi zidzachititsa kuti anthu apeze moyo wosatha kudzera mwa Yesu Khristu Ambuye wathu.+

  • Aroma 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chifukwa malipiro a uchimo ndi imfa,+ koma mphatso imene Mulungu amapereka ndi moyo wosatha+ kudzera mwa Khristu Yesu Ambuye wathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena