-
Numeri 19:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Munthu wodetsedwayo amutapireko phulusa la nsembe yamachimo imene inawotchedwa ija. Phulusalo aliike mʼchiwiya nʼkuthiramo madzi akumtsinje.
-