Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:6-8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Nsembe zanyama komanso nsembe zina, simunazifune.*+

      Koma munatsegula makutu anga kuti ndimve.+

      Simunapemphe nsembe zopsereza ndi nsembe zamachimo.+

       7 Ndiyeno ine ndinati: “Taonani, ine ndabwera.

      Mumpukutu* munalembedwa za ine.+

       8 Ndimasangalala* kuchita zimene mumafuna, inu Mulungu wanga,+

      Ndipo chilamulo chanu chili mumtima mwanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena