Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 5:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi akasupe ako amwazike panja?

      Ndipo kodi mitsinje yako ya madzi imwazike mʼmabwalo amumzinda?+

  • Miyambo 5:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiye mwana wanga, kodi pali chifukwa chilichonse choti uzisangalalira ndi mkazi wamakhalidwe oipa,*

      Kapena choti uzikumbatirira chifuwa cha mkazi wachiwerewere?*+

  • Mateyu 5:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Koma ine ndikukuuzani kuti aliyense woyangʼanitsitsa mkazi+ mpaka kumulakalaka, wachita naye kale chigololo mumtima mwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena