Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chifukwa ngakhale Khristu sankachita zinthu zodzikondweretsa yekha,+ koma anachita zimene Malemba amanena kuti: “Chipongwe cha anthu amene amakunyozani chandigwera.”+

  • 2 Akorinto 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho ndimasangalala ndi kufooka, kunyozedwa, kusowa zofunika pa moyo, kuzunzidwa ndiponso zovuta zina chifukwa cha Khristu. Chifukwa pamene ndili wofooka, mʼpamene ndimakhala wamphamvu.+

  • 1 Petulo 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndinu osangalala*+ ngati anthu akukunyozani chifukwa cha dzina la Khristu chifukwa zimenezi zikusonyeza kuti mzimu woyera wa Mulungu komanso ulemerero wake zili pa inu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena