Yesaya 40:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Iye adzasamalira* gulu la nkhosa zake ngati mʼbusa.+ Ndi dzanja lake, adzasonkhanitsa pamodzi ana a nkhosa,Ndipo adzawanyamulira pachifuwa pake. Nkhosa zimene zikuyamwitsa adzazitsogolera mwachikondi.+ Yohane 21:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Kenako anamufunsa kachiwiri kuti: “Simoni mwana wa Yohane, kodi ine umandikonda?” Iye anamuyankha kuti: “Inde Ambuye, inunso mukudziwa kuti ndimakukondani kwambiri.” Pamenepo anati: “Weta ana a nkhosa anga.”+ Machitidwe 20:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Muzidziyangʼanira nokha+ komanso kusamalira gulu lonse la nkhosa, limene mzimu woyera wakuikani kuti muziliyangʼanira,+ kuti muwete mpingo wa Mulungu,+ umene anaugula ndi magazi a Mwana wake weniweni.+
11 Iye adzasamalira* gulu la nkhosa zake ngati mʼbusa.+ Ndi dzanja lake, adzasonkhanitsa pamodzi ana a nkhosa,Ndipo adzawanyamulira pachifuwa pake. Nkhosa zimene zikuyamwitsa adzazitsogolera mwachikondi.+
16 Kenako anamufunsa kachiwiri kuti: “Simoni mwana wa Yohane, kodi ine umandikonda?” Iye anamuyankha kuti: “Inde Ambuye, inunso mukudziwa kuti ndimakukondani kwambiri.” Pamenepo anati: “Weta ana a nkhosa anga.”+
28 Muzidziyangʼanira nokha+ komanso kusamalira gulu lonse la nkhosa, limene mzimu woyera wakuikani kuti muziliyangʼanira,+ kuti muwete mpingo wa Mulungu,+ umene anaugula ndi magazi a Mwana wake weniweni.+