Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 53:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye ananyozedwa ndipo anthu ankamupewa,+

      Anali munthu amene kupweteka ankakudziwa bwino* ndipo matenda ankawadziwa.

      Zinali ngati kuti nkhope yake yabisika kwa ife.*

      Ananyozedwa ndipo tinkamuona ngati wopanda pake.+

  • Yohane 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma iwo anafuula kuti: “Muthane naye! Muthane naye! Apachikidwe ameneyo!”* Pilato anawafunsa kuti: “Kodi ndipachike mfumu yanu?” Ansembe aakulu anayankha kuti: “Tilibe mfumu ina koma Kaisara.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena